Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 28:23 - Buku Lopatulika

23 Nupangire pa chapachifuwa mphete ziwiri zagolide, ndi kuzika mphete ziwirizo pansonga zake ziwiri za chapachifuwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Nupangire pa chapachifuwa mphete ziwiri zagolide, ndi kuzika mphete ziwirizo pa nsonga zake ziwiri za chapachifuwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Upangenso mphete ziŵiri, ndipo uzilumikize pa ngodya zam'mwamba za chovala chapachifuwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Upangenso mphete ziwiri zagolide ndipo uzimangirire pa ngodya ziwiri za pa chovala chapachifuwa.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 28:23
3 Mawu Ofanana  

Upangenso maunyolo pa chapachifuwa ngati zingwe, ntchito yopota, ya golide woona.


Numange maunyolo awiri opota agolide ku mphete ziwirizo pansonga pake pa chapachifuwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa