Eksodo 28:10 - Buku Lopatulika10 maina asanu ndi limodzi pamwala wina, ndi maina asanu ndi limodzi otsala pamwala unzake, mwa kubadwa kwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 maina asanu ndi limodzi pa mwala wina, ndi maina asanu ndi limodzi otsala pa mwala unzake, mwa kubadwa kwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Pa mwala umodzi ulembepo maina asanu ndi limodzi, ndipo pa mwala winawo uchitenso chimodzimodzi. Ulembe mainawo motsatana malinga nkubadwa kwa ana a Israelewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Mayina asanu ndi limodzi akhale pa mwala umodzi, ndipo mayina asanu ndi limodzi pa mwala winawo motsata mabadwidwe awo. Onani mutuwo |