Eksodo 28:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo utenge miyala iwiri yaberulo, nulochepo maina a ana a Israele; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo utenge miyala iwiri yaberulo, nulochepo maina a ana a Israele; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Utenge miyala iŵiri ya onikisi, ndipo ulembepo maina a ana a Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Utenge miyala iwiri ya onikisi ndipo uzokotepo mayina a ana a Israeli. Onani mutuwo |
Ndi mphamvu yanga yonse tsono ndakonzeratu nyumba ya Mulungu wanga, golide wa zija zagolide ndi siliva wa zija zasiliva, ndi mkuwa wa zija zamkuwa, chitsulo cha zija zachitsulo, ndi mtengo wa zija zamtengo, miyala yaberulo, ndi miyala yoikika, miyala yokometsera, ndi ya mawangamawanga, ndi miyala ya mtengo wake ya mitundumitundu ndi miyala yansangalabwe yochuluka.