Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 27:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo m'kupingasa kwake kwa bwalo pa mbali ya kum'mawa, kum'mawa, mukhale mikono makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo m'kupingasa kwake kwa bwalo pa mbali ya kum'mawa, kum'mawa, mukhale mikono makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Chakuvuma, komwe kuli chipata chake, bwalolo likhalenso mamita 23 muufupi mwake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Mbali yakummawa, kotulukira dzuwa, kutalika kwa bwalo kukhale mamita 23.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 27:13
2 Mawu Ofanana  

Ndipo m'kupingasa kwa bwaloli pa mbali ya kumadzulo mukhale nsalu zotchingira za mikono makumi asanu; nsichi zake zikhale khumi, ndi makamwa ao khumi.


Ndi nsalu zotchingira za pa mbali imodzi ya kuchipata zikhale za mikono khumi ndi isanu; nsichi zake zikhale zitatu, ndi makamwa ao atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa