Eksodo 26:36 - Buku Lopatulika36 Ndipo uziomba nsalu yotsekera pa khomo la hema, ya lakuda, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa, ntchito ya wopikula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Ndipo uziomba nsalu yotsekera pa khomo la hema, ya lakuda, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa, ntchito ya wopikula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 “Pa chipata choloŵera m'chihemamo, uikepo nsalu yochingira yobiriŵira, yofiirira ndi yofiira, ndi ya bafuta wosalala, wopikidwa bwino ndi wopetedwa mwaluso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 “Pa chipata cholowera mu chihema, uyikepo nsalu yamtundu wamtambo, wapepo ndi ofiira, yomwe ndi yofewa ndi yosalala, yopetedwa bwino ndi amisiri aluso. Onani mutuwo |