Eksodo 26:28 - Buku Lopatulika28 Ndi mtanda wa pakati pa matabwa ufikire kuthungo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndi mtanda wa pakati pa matabwa ufikire kuthungo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Mtanda wa pakati penipeni pa mafulemuwo ugwire mafulemu onse, kuyambira ku mapeto mpaka ku mapeto. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Mtanda wapakati pa maferemuwo uchokere pa maferemu a mbali ina mpaka mbali inanso. Onani mutuwo |