Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 25:39 - Buku Lopatulika

39 Achipange ichi ndi zipangizo izi zonse za talente wa golide woona.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Achipange ichi ndi zipangizo izi zonse za talente wa golide woona.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Choikaponyalecho ndi zipangizo zonse uzipange ndi golide wolemera makilogaramu 34.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Choyikapo nyale ndi zipangizo zonse zipangidwe ndi golide wabwino kwambiri wolemera makilogalamu 34.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 25:39
2 Mawu Ofanana  

Ndipo mbano zake, ndi zoolera zake, zikhale za golide woona.


Ndipo uyang'anire uzipanga monga mwachifaniziro chao, chimene anakuonetsa m'phirimo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa