Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 25:38 - Buku Lopatulika

38 Ndipo mbano zake, ndi zoolera zake, zikhale za golide woona.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Ndipo mbano zake, ndi zoolera zake, zikhale za golide woona.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Mbano zogwirira, pamodzi ndi timbale take tomwe, zikhale za golide wabwino kwambiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Mbaniro ndi zowolera phulusa zikhale zagolide wabwino kwambiri.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 25:38
10 Mawu Ofanana  

ndi zikho, ndi zozimira nyali, ndi mbale, ndi zipande, ndi zopalira moto za golide woyengetsa, ndi zomangira zitseko zagolide, za zitseko za chipinda cha m'katimo, malo opatulika kwambiri, ndiponso za zitseko za nyumba ya Kachisi.


Koma sanapangire nyumba ya Yehova mbale zasiliva, mbano, mbale zowazira, malipenga, zotengera zilizonse zagolide, kapena zotengera zilizonse zasiliva, kuzipanga ndi ndalama adabwera nazo kunyumba ya Yehova;


Nachotsanso miphika, ndi zoolera, ndi zozimira nyali, ndi zipande, ndi zipangizo zonse zamkuwa zimene anatumikira nazo.


ndi maluwa, ndi nyali, ndi mbano zagolide, ndiwo golide wangwiro;


Ndipo uzipanga nyali zake, zisanu ndi ziwiri; ndipo ayatse nyali zake, ziwale pandunji pake.


Achipange ichi ndi zipangizo izi zonse za talente wa golide woona.


Ndipo anapanga nyali zake zisanu ndi ziwiri ndi mbano zake, ndi zoolera zake, za golide woona.


Pompo anaulukira kwa ine mmodzi wa aserafi, ali nalo khala lamoto m'dzanja mwake, limene analichotsa ndi mbaniro paguwa la nsembe;


Ndiponso miphika, ndi zoolera, ndi mbano zao, ndi mbale, ndi zipande, ndi zipangizo zonse zamkuwa zimene anatumikira nazo, anazichotsa.


Ndipo atenge nsalu yamadzi, ndi kuphimba choikaponyali younikira, ndi nyali zake, ndi mbano zake, ndi zoolera zake, ndi zotengera zake zonse za mafuta zogwira nazo ntchito yake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa