Eksodo 25:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo uzipanga choikaponyali cha golide woona; choikapocho chisulidwe mapangidwe ake, tsinde lake ndi thupi lake; zikho zake, mitu yake, ndi maluwa ake zikhale zochokera m'mwemo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo uzipanga choikapo nyali cha golide woona; choikapocho chisulidwe mapangidwe ake, tsinde lake ndi thupi lake; zikho zake, mitu yake, ndi maluwa ake zikhale zochokera m'mwemo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 “Upange choikaponyale cha golide wabwino kwambiri. Tsinde lake ndi thunthu lake zikhale zagolide, ndipo uchisule ndi nyundo. Zikho zake, ndiye kuti nkhunje ndi maluŵa ake, zonsezo zipangidwire kumodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 “Upange choyikapo nyale chagolide wabwino kwambiri. Tsinde lake ndi mphanda zake zikhale zosulidwa ndi nyundo. Zikho zake zokhala ndi mphukira ndi maluwa ake zipangidwire kumodzi. Onani mutuwo |