Eksodo 25:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo uzipanga mbale zake, ndi zipande zake, ndi mitsuko yake, ndi zikho zake zakuthira nazo; uzipanga za golide woona. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo uzipanga mbale zake, ndi zipande zake, ndi mitsuko yake, ndi zikho zake zakuthira nazo; uzipanga za golide woona. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Upange mbale ndi zipande zofunika popereka lubani, ndiponso mitsuko ndi mabeseni ofunika pa zopereka za chakumwa. Zonsezi zikhale za golide wabwino kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Upange mbale ndi zipande zagolide wabwino, pamodzinso ndi mitsuko ndi mabeseni zogwiritsa ntchito popereka nsembe. Onani mutuwo |