Eksodo 25:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo uzipanga mphiko za mtengo wakasiya, ndi kuzikuta ndi golide, kuti anyamulire nazo gome. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo uzipanga mphiko za mtengo wakasiya, ndi kuzikuta ndi golide, kuti anyamulire nazo gome. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Upange mphiko zonyamulira za mtengo wa kasiya, ndipo uzikute ndi golide. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Upange nsichi zamtengo wa mkesha ndi kuzikuta ndi golide kuti azinyamulira tebulolo. Onani mutuwo |