Eksodo 24:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo anati kwa akulu, Tilindeni kuno kufikira tidzabwera kwa inu; ndipo taonani, Aroni ndi Huri ali nanu; munthu akakhala ndi mlandu abwere kwa iwowa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo anati kwa akulu, Tilindeni kuno kufikira tidzabwera kwa inu; ndipo taonani, Aroni ndi Huri ali nanu; munthu akakhala ndi mlandu abwere kwa iwowa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Iyeyo anali atauza atsogoleri aja kuti, “Batiyembekezani pano, mpaka tidzakupezeni. Aroni ndi Huri muli nawo pompano. Amene akhale ndi milandu, apite kwa iwowo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Apa nʼkuti Mose atawawuza akuluakulu aja kuti, “Mudikire pano mpaka titabweranso. Aaroni ndi Huri ali nanu, aliyense amene ali ndi milandu apite kwa iwo.” Onani mutuwo |