Eksodo 23:1 - Buku Lopatulika1 Usatola mbiri yopanda pake; usathandizana naye woipa ndi kukhala mboni yochititsa chiwawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Usatola mbiri yopanda pake; usathandizana naye woipa ndi kukhala mboni yochititsa chiwawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 “Usachite umboni wonama. Munthu wolakwa usamthandize pakumchitira umboni wonama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 “Usafalitse mbiri yabodza. Usathandize munthu wolakwa pomuchitira umboni wonama. Onani mutuwo |