Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 22:2 - Buku Lopatulika

2 Akampeza wakuba alimkuboola, nakamkantha kotero kuti wafa, palibe chamwazi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Akampeza wakuba alimkuboola, nakamkantha kotero kuti wafa, palibe chamwazi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 “Ngati mbala ipezeka ikuthyola nyumba ndipo ikanthidwa nkufa, asalipsire magazi chifukwa cha mbalayo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 “Ngati mbala ipezeka ikuthyola nyumba ndipo imenyedwa nʼkufa, amene wapha mbalayo sanalakwe.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 22:2
11 Mawu Ofanana  

Kukacha auka wambanda, napha wosauka ndi waumphawi; ndi usiku asanduka mbala.


Kuli mdima aboola nyumba, usana adzitsekera, osadziwa kuunika.


Anawapirikitsa pakati pa anthu, awafuulira ngati kutsata mbala.


Ndiponso m'nsalu zako wapezeka mwazi wa miyoyo ya aumphawi osachimwa; sunawapeze pakuboola, koma ponsepo.


M'mene ndichiritsa Israele, mphulupulu ya Efuremu ivumbuluka, ndi zoipa za Samariya; pakuti achita bodza, ndipo mkhungu alowa m'nyumba, ndi gulu la mbala lilanda kubwalo.


Alumphira mzinda, athamanga palinga, akwerera nyumba, alowera pamazenera ngati khungu.


nakampeza wolipsa mwazi kunja kwa malire a mzinda wake wothawirako, ndipo wolipsa mwazi akapha wakupha munthu, alibe kuchimwira mwazi;


Koma dziwani ichi, kuti mwini nyumba akadadziwa nthawi yiti mbala ikudza, iye akadadikira, ndipo sakadalola kuti nyumba yake ibooledwe.


Pakuti inu nokha mudziwa bwino kuti tsiku la Ambuye lidzadza monga mbala usiku.


Pakuti asamve zowawa wina wa inu ngati wambanda, kapena mbala, kapena wochita zoipa, kapena ngati wodudukira;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa