Eksodo 22:2 - Buku Lopatulika2 Akampeza wakuba alimkuboola, nakamkantha kotero kuti wafa, palibe chamwazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Akampeza wakuba alimkuboola, nakamkantha kotero kuti wafa, palibe chamwazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Ngati mbala ipezeka ikuthyola nyumba ndipo ikanthidwa nkufa, asalipsire magazi chifukwa cha mbalayo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Ngati mbala ipezeka ikuthyola nyumba ndipo imenyedwa nʼkufa, amene wapha mbalayo sanalakwe. Onani mutuwo |