Eksodo 22:17 - Buku Lopatulika17 Atate wake akakana konse kumpatsa iye, alipe ndalama monga mwa cholipa cha anamwali. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Atate wake akakana konse kumpatsa iye, alipe ndalama monga mwa cholipa cha anamwali. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Koma ngati bambo wake wa namwaliyo akana kuti mwana wakeyo asakwatiwe, munthuyo adzangolipirabe ndalama za chiwongo cha namwali. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ngati abambo ake akanitsitsa kwamtuwagalu kumupereka kuti amukwatire, munthuyo aperekebe malowolo woyenera namwaliyo. Onani mutuwo |