Eksodo 22:12 - Buku Lopatulika12 Koma ngati chidabedwa kwaoko ndithu, alipe kwa mwiniyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Koma ngati chidabedwa kwaoko ndithu, alipe kwa mwiniyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Koma ngati choŵetacho chidabedwa, mwiniwakeyo adzalipidwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Koma ngati chiwetocho chinabedwa, iye ayenera kubwezera mwini wakeyo. Onani mutuwo |