Eksodo 22:13 - Buku Lopatulika13 Ngati chajiwa ndithu, abwere nacho chikhale mboni; asalipe pa chojiwacho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ngati chajiwa ndithu, abwere nacho chikhale mboni; asalipe pa chojiwacho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ngati chidajiwa ndi zilombo, atengeko zotsalira zake kuti zikhale mboni, koma asalipire chimene chidajiwa ndi zilombocho. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ngati chinagwidwa ndi zirombo, iye ayenera kubweretsa zotsalira ngati umboni ndipo sadzalipira kanthu. Onani mutuwo |