Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 22:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Koma ngati chiwetocho chinabedwa, iye ayenera kubwezera mwini wakeyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

12 Koma ngati chidabedwa kwaoko ndithu, alipe kwa mwiniyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Koma ngati chidabedwa kwaoko ndithu, alipe kwa mwiniyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Koma ngati choŵetacho chidabedwa, mwiniwakeyo adzalipidwa.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 22:12
4 Mawu Ofanana  

Chiweto chikakhadzulidwa ndi chirombo, sindinkabwera nacho kwa inu. Ineyo ndinkalipira. Inuyo munkandilipiritsa kalikonse kobedwa masana kapena usiku.


ndiye kuti anthu awiriwo ayenera kulumbira pamaso pa Mulungu kuti asatenge chinthu cha mnzake. Zikatero mwini katundu uja avomereze zimenezi ndipo asabwezeredwe kanthu.


Ngati chinagwidwa ndi zirombo, iye ayenera kubweretsa zotsalira ngati umboni ndipo sadzalipira kanthu.


“Ngati munthu asungitsidwa ndi mnzake ndalama kapena katundu, ndipo zinthu zija nʼkubedwa mʼnyumba mwake, wakubayo ngati agwidwa, ayenera kubwezera kawiri chobedwacho.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa