Eksodo 22:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Koma ngati chiwetocho chinabedwa, iye ayenera kubwezera mwini wakeyo. Onani mutuwoBuku Lopatulika12 Koma ngati chidabedwa kwaoko ndithu, alipe kwa mwiniyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Koma ngati chidabedwa kwaoko ndithu, alipe kwa mwiniyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Koma ngati choŵetacho chidabedwa, mwiniwakeyo adzalipidwa. Onani mutuwo |