Eksodo 21:5 - Buku Lopatulika5 Koma mnyamatayo akanenetsa, Ndikonda mbuye wanga, mkazi wanga, ndi ana anga; sindituluka waufulu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma mnyamatayo akanenetsa, Ndikonda mbuye wanga, mkazi wanga, ndi ana anga; sindituluka waufulu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma kapoloyo akanena kuti, ‘Ndimakonda mbuyanga, mkazi wanga ndi ana anga, sindifuna kuti ndimasulidwe,’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 “Koma ngati kapoloyo alengeza kuti, ‘Ine sindikufuna kumasulidwa chifukwa ndimakonda mbuye wanga, mkazi wanga ndi ana,’ Onani mutuwo |