Eksodo 21:5 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 “Koma ngati kapoloyo alengeza kuti, ‘Ine sindikufuna kumasulidwa chifukwa ndimakonda mbuye wanga, mkazi wanga ndi ana,’ Onani mutuwoBuku Lopatulika5 Koma mnyamatayo akanenetsa, Ndikonda mbuye wanga, mkazi wanga, ndi ana anga; sindituluka waufulu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma mnyamatayo akanenetsa, Ndikonda mbuye wanga, mkazi wanga, ndi ana anga; sindituluka waufulu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma kapoloyo akanena kuti, ‘Ndimakonda mbuyanga, mkazi wanga ndi ana anga, sindifuna kuti ndimasulidwe,’ Onani mutuwo |