Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 21:5 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 “Koma ngati kapoloyo alengeza kuti, ‘Ine sindikufuna kumasulidwa chifukwa ndimakonda mbuye wanga, mkazi wanga ndi ana,’

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

5 Koma mnyamatayo akanenetsa, Ndikonda mbuye wanga, mkazi wanga, ndi ana anga; sindituluka waufulu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Koma mnyamatayo akanenetsa, Ndikonda mbuye wanga, mkazi wanga, ndi ana anga; sindituluka waufulu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Koma kapoloyo akanena kuti, ‘Ndimakonda mbuyanga, mkazi wanga ndi ana anga, sindifuna kuti ndimasulidwe,’

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 21:5
5 Mawu Ofanana  

Ngati bwana wake amupatsa mkazi ndipo mkaziyo anabereka ana aamuna kapena aakazi, mkazi ndi anawo adzakhala a bwanayo ndipo mwamuna yekhayo ndiye adzamasulidwe.


mbuye wakeyo abwere naye kwa Yehova. Abwere naye pa chitseko kapena pa mphuthu zachitseko ndipo abowole khutu lake ndi chitsulo. Ndipo iye adzakhala kapolo wake moyo wake wonse.


Inu Yehova Mulungu wathu, ngakhale takhala tikulamulidwa ndi ena mʼmalo mwanu, koma ife timalemekeza dzina lanu lokha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa