Eksodo 21:30 - Buku Lopatulika30 Akamuikira dipo, azipereka chiombolo cha moyo wake monga mwa zonse adamuikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Akamuikira dipo, azipereka chiombolo cha moyo wake monga mwa zonse adamuikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Koma ngati amlamula kuti adziwombole, adzayenera kulipira ndalama, kuti apulumutse moyo wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Koma ngati wauzidwa kuti alipire, iye apereke zimene wauzidwazo kuti awombole moyo wake. Onani mutuwo |