Eksodo 21:31 - Buku Lopatulika31 Ingakhale yatunga mwana wamwamuna kapena wamkazi, aichitire monga mwa chiweruzo ichi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ingakhale yatunga mwana wamwamuna kapena wamkazi, aichitire monga mwa chiweruzo ichi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Ng'ombe ikapha mnyamata kapena mtsikana, lamulo lake ndi lomwelo ndithu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Lamulo ili ligwirenso ntchito ngati ngʼombeyo yagunda mwana wamwamuna kapena wamkazi. Onani mutuwo |