Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 21:3 - Buku Lopatulika

3 Akalowa ali yekha azituluka ali yekha; akakhala ndi mkazi, mkazi wake azituluka naye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Akalowa ali yekha azituluka ali yekha; akakhala ndi mkazi, mkazi wake azituluka naye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Akakhala kuti anali yekha, adzachokanso yekha. Koma ngati anali ndi mkazi pobwerapo, mkazi wakeyo adzapita naye limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Ngati anabwera yekha, amasulidwenso yekha. Koma ngati anali ndi mkazi pamene ankabwera, mkaziyo apite nayenso.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 21:3
5 Mawu Ofanana  

Ukagula mnyamata Muhebri, azigwira ntchito zaka zisanu ndi chimodzi; koma chachisanu ndi chiwiri azituluka waufulu chabe.


Akampatsa mkazi mbuye wake, ndipo akambalira ana aamuna ndi aakazi, mkaziyo ndi ana ake azikhala a mbuye wake, ndipo azituluka ali yekha.


Ndipo munthu akagulitsa mwana wake wamkazi akhale mdzakazi, iyeyu asatuluke monga amatuluka anyamata.


Pamenepo azituluka kukuchokera, iye ndi ana ake omwe, nabwerere ku mbumba yake; abwerere ku dziko laolao la makolo ake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa