Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 21:27 - Buku Lopatulika

27 Ndipo akagulula dzino la mnyamata wake, kapena dzino la mdzakazi wake, azimlola amuke waufulu chifukwa cha dzino lake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Ndipo akagulula dzino la mnyamata wake, kapena dzino la mdzakazi wake, azimlola amuke waufulu chifukwa cha dzino lake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Akamchotsa dzino, ammasule kapoloyo, kuti akhale mfulu chifukwa cha dzinolo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Ndipo ngati agulula dzino la wantchito wamwamuna kapena mdzakazi, wantchitoyo amasulidwe ngati malipiro a dzino lake.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 21:27
2 Mawu Ofanana  

Munthu akampanda mnyamata wake, kapena mdzakazi wake, padiso, nalithudzula, azimlola amuke waufulu chifukwa cha diso lake.


Ng'ombe ikatunga mwamuna kapena mkazi, nafa, aiponyetu miyala ng'ombeyo, osadya nyama yake; koma mwini ng'ombeyo azimasuka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa