Eksodo 21:26 - Buku Lopatulika26 Munthu akampanda mnyamata wake, kapena mdzakazi wake, padiso, nalithudzula, azimlola amuke waufulu chifukwa cha diso lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Munthu akampanda mnyamata wake, kapena mdzakazi wake, padiso, nalithudzula, azimlola amuke waufulu chifukwa cha diso lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 “Munthu akamenya kapolo wamwamuna kapena wamkazi pa diso, nkulikoloola disolo, ammasule kapoloyo, kuti akhale mfulu chifukwa cha disolo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 “Ngati munthu amenya wantchito wake wa mwamuna kapena mdzakazi wake pa diso ndi kuliwononga, wantchitoyo amasulidwe ngati malipiro a diso lake. Onani mutuwo |