Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 21:22 - Buku Lopatulika

22 Akayambana amuna, nakakantha mkazi ali ndi pakati, kotero kuti abala, koma alibe kuphwetekwa; alipe ndithu, monga momwe amtchulira mwamuna wa mkaziyo; apereke monga anena oweruza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Akayambana amuna, nakakantha mkazi ali ndi pakati, kotero kuti abala, koma alibe kuphwetekwa; alipe ndithu, monga momwe amtchulira mwamuna wa mkaziyo; apereke monga anena oweruza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 “Anthu aamuna akamayambana, ndipo nkupweteka mai wapathupi, maiyo napititsa padera, koma osafa, amene adampwetekayo adzalipira mtengo uliwonse umene mwamuna wa maiyo angadzatchule. Ndipo adzalipira monga momwe anthu oweruza anganenere.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 “Ngati anthu akumenyana ndi kupweteka mayi woyembekezera, mayiyo napita padera, koma osavulala, wolakwayo ayenera kulipira chilichonse chimene mwamuna wake wa mkaziyo adzalamula ndipo bwalo lamilandu lavomereza.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 21:22
3 Mawu Ofanana  

Akamuikira dipo, azipereka chiombolo cha moyo wake monga mwa zonse adamuikira.


Mudziikire oweruza ndi akapitao m'midzi yanu yonse imene Yehova Mulungu wanu akupatsani, monga mwa mafuko anu; ndipo aweruze anthu ndi chiweruzo cholungama.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa