Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 21:21 - Buku Lopatulika

21 Koma akakhala wosafa tsiku limodzi kapena awiri, asalangike, pakuti ndiye ndalama ya mbuye wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Koma akakhala wosafa tsiku limodzi kapena awiri, asalirike, pakuti ndiye ndalama ya mbuye wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Koma kapoloyo akakhala moyo tsiku lathunthu kapena masiku aŵiri, mbuyakeyo asalangidwe. Kapoloyo ndi chuma cha mbuyakeyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Koma ngati kapolo uja akhala ndi moyo tsiku lonse kapena masiku awiri, ndiye kuti mbuye uja asalangidwe chifukwa kapolo ndi chuma chake.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 21:21
2 Mawu Ofanana  

Munthu akakantha mnyamata wake, kapena mdzakazi wake, ndi ndodo, ndipo akafa padzanja pake; ameneyo alangidwe ndithu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa