Eksodo 21:20 - Buku Lopatulika20 Munthu akakantha mnyamata wake, kapena mdzakazi wake, ndi ndodo, ndipo akafa padzanja pake; ameneyo alangidwe ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Munthu akakantha mnyamata wake, kapena mdzakazi wake, ndi ndodo, ndipo akafa padzanja pake; ameneyo aliridwe ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 “Munthu akamenya kapolo wake wamwamuna kapena wamkazi ndi ndodo, ndipo kapoloyo afera pomwepo, munthuyo adzalangidwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 “Ngati munthu amenya kapolo wake wamwamuna kapena mdzakazi ndi ndodo, kapolo uja ndikufa chifukwa cha kumenyedwako, munthuyo ayenera kulangidwa. Onani mutuwo |