Eksodo 21:18 - Buku Lopatulika18 Akalimbana amuna, ndipo wina akakantha mnzake ndi mwala, kapena ndi nkhonya, wosafa iye, koma wakhulungira pakama; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Akalimbana amuna, ndipo wina akakantha mnzake ndi mwala, kapena ndi nkhonya, wosafa iye, koma wakhulungira pakama; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 “Anthu akamenyana, ndipo wina mwa iwowo amenya mnzake ndi mwala kapena nkhonya, koma osamupha mnzakeyo, munthu womenyedwayo akadwala nakagona pa bedi, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 “Ngati anthu awiri akangana ndipo wina amenya mnzake ndi mwala kapena nkhonya koma wosamupha, womenyedwayo akadwala nagona pa bedi, Onani mutuwo |