Eksodo 20:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo ukandimangira guwa la nsembe lamiyala, usalimanga ndi miyala yosema; ukakwezapo chosemera chako, waliipsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo ukandimangira guwa la nsembe lamiyala, usalimanga ndi miyala yosema; ukakwezapo chosemera chako, waliipsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Mukadzandimangira guwa lamiyala, miyala yake musadzaseme, chifukwa mukadzaisema ndi chitsulo chosemera, mudzaipitsa guwalo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Ngati mudzandimangira guwa lansembe lamiyala, musagwiritse ntchito miyala yosema, pakuti mudzalidetsa mukadzagwiritsa ntchito zida. Onani mutuwo |