Eksodo 20:26 - Buku Lopatulika26 Kapena usakwere ndi makwerero ku guwa langa la nsembe, kuti angaoneke maliseche ako pamenepo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Kapena usakwere ndi makwerero ku guwa langa la nsembe, kuti angaoneke maliseche ako pamenepo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Popita ku guwa langa, musadzaponde pa makwerero, kuti maliseche anu angaonekere.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Musamakwere pa makwerero popita pa guwa langa lansembe kuti mungaonetse maliseche anu. Onani mutuwo |