Eksodo 2:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo Mose anavomera kukhala naye munthuyo; ndipo anampatsa Mose mwana wake wamkazi Zipora. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo Mose anavomera kukhala naye munthuyo; ndipo anampatsa Mose mwana wake wamkazi Zipora. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Choncho Mose adavomera kukhala nao komweko, ndipo Reuele adapatsa Moseyo mwana wake Zipora kuti akhale mkazi wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Mose anavomera kukhala ndi Reueli, ndipo anamupatsa Zipora kuti akhale mkazi wake. Onani mutuwo |