Eksodo 2:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo anati iwo, Munthu Mwejipito anatilanditsa m'manja a abusa, natitungiranso madzi okwanira, namwetsa gululi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo anati iwo, Munthu Mwejipito anatilanditsa m'manja a abusa, natitungiranso madzi okwanira, namwetsa gululi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Iwo aja adayankha kuti, “Mwejipito wina ndiye amene watitchinjiriza kwa abusa, ndipo watitungira madzi omwetsa zoŵeta zonsezi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Atsikanawo anayankha kuti, “Mwigupto wina ndiye watilanditsa kwa abusa. Ndiponso anatitungira madzi ndi kumwetsa ziweto zathu.” Onani mutuwo |