Eksodo 19:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Taona, ndikudza kwa iwe mu mtambo wakuda bii, kuti anthu amve pamene ndilankhula ndi iwe, ndi kuti akuvomereze nthawi zonse. Pakuti Mose adauza Yehova mau a anthuwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Taona, ndikudza kwa iwe mu mtambo wakuda bii, kuti anthu amve pamene ndilankhula ndi iwe, ndi kuti akuvomereze nthawi zonse. Pakuti Mose adauza Yehova mau a anthuwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Chauta adauza Mose kuti, “Ndikubwera kwa iwe mu mtambo wochindikira, kuti anthuwo azidzandimva ndikamalankhula ndi iwe, ndiponso kuti adzakhulupirire nthaŵi zonse.” Tsono Mose adauza Chauta zimene anthu adanena. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Yehova anati kwa Mose, “Ine ndibwera kwa iwe mu mtambo wakuda kuti anthu adzandimve ndikuyankhula ndi iwe. Choncho adzakukhulupirira nthawi zonse.” Kenaka Mose anawuza Yehova zimene anthu ananena. Onani mutuwo |