Eksodo 19:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Muka kwa anthuwo, nuwapatulitse lero ndi mawa, ndipo atsuke zovala zao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Muka kwa anthuwo, nuwapatulitse lero ndi mawa, ndipo atsuke zovala zao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Chauta adauza Mose kuti, “Pita kwa anthuwo, ndipo uŵayeretse lero ndi maŵa. Achape zovala zao, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndipo Yehova anati kwa Mose, “Pita kwa anthu onse ndi kuwayeretsa lero ndi mawa. Achape zovala zawo Onani mutuwo |