Eksodo 19:6 - Buku Lopatulika6 ndipo ndidzakuyesani ufumu wanga wa ansembe, ndi mtundu wopatulika. Awa ndi mau amene ukalankhule ndi ana a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndipo ndidzakuyesani ufumu wanga wa ansembe, ndi mtundu wopatulika. Awa ndi mau amene ukalankhule ndi ana a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndipo inu mudzakhala anthu onditumikira Ine ngati ansembe, ndiponso ngati mtundu woyera. Tsono ukaŵauze mau ameneŵa Aisraele.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 inu mudzakhala ansembe achifumu ndi mtundu woyera mtima. Awa ndi mawu amene uyenera kuwawuza Aisraeli.” Onani mutuwo |