Eksodo 19:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo Yehova anati kwa iye, Muka, tsika; nukwere iwe ndi Aroni pamodzi ndi iwe; koma ansembe ndi anthu asapyole kukwera kwa Yehova, angawapasule. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo Yehova anati kwa iye, Muka, tsika; nukwere iwe ndi Aroni pamodzi ndi iwe; koma ansembe ndi anthu asapyole kukwera kwa Yehova, angawapasule. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Tsono Chauta adauza Moseyo kuti, “Tsika pansi, ndipo ukamtenge Aroni, ubwere naye kuno. Koma ansembe pamodzi ndi anthu asabzole malirewo kubwera kwa Ine kuno, kuti ndingadzaŵalange.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Yehova anayankha, “Tsika ukamutenge Aaroni. Koma ansembe ndi anthu asayesere kubzola malire kuti abwere kwa Yehova chifukwa Iye adzawalanga.” Onani mutuwo |