Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 19:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo Mose anati kwa Yehova, Anthu sangathe kukwera m'phiri la Sinai; pakuti Inu mwatichenjeza, ndi kuti, Lemba malire m'phirimo, ndi kulipatula.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo Mose anati kwa Yehova, Anthu sangathe kukwera m'phiri la Sinai; pakuti Inu mwatichenjeza, ndi kuti, Lemba malire m'phirimo, ndi kulipatula.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Mose adayankha Chauta kuti, “Anthuwo sangakwere ai, chifukwa mudachenjezeratu kuti, ‘Mulembe malire kuzungulira phirilo, ndipo mulipatule kuti likhale loyera.’ ”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Mose anati kwa Yehova, “Anthu sangakwere phiri la Sinai chifukwa inu munatichenjeza. Lembani malire kuzungulira phiri ndipo mulipatule kuti likhale loyera.”

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 19:23
3 Mawu Ofanana  

Ndipo ukalembere anthu malire pozungulira, ndi kuti, Muzichenjera musakwere m'phiri, musakhudza malire ake; wokhudza phirilo adzaphedwa ndithu;


Ndipo Yehova anati kwa iye, Muka, tsika; nukwere iwe ndi Aroni pamodzi ndi iwe; koma ansembe ndi anthu asapyole kukwera kwa Yehova, angawapasule.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa