Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 18:6 - Buku Lopatulika

6 nati kwa Mose, Ine mpongozi wako Yetero ndadza kwa iwe, ndi mkazi wako, ndi ana ake omwe awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 nati kwa Mose, Ine mpongozi wako Yetero ndadza kwa iwe, ndi mkazi wako, ndi ana ake omwe awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Munthu wina adakauza Mose kuti, “Mpongozi wanu Yetero akubwera ndi mkazi wanu ndi ana anu aŵiri aamuna.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Yetero anali atatumiza uthenga kwa Mose kuti, “Ine Yetero, mpongozi wako, ndikubwera ndi mkazi wako ndi ana ake awiri.”

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 18:6
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Yetero, mpongozi wa Mose, anadza ndi ana ake aamuna ndi mkazi wake kwa Mose kuchipululu kumene adamangako, paphiri la Mulungu;


Ndipo Mose anatuluka kukakomana ndi mpongozi wake, nawerama, nampsompsona; nafunsana ali bwanji, nalowa m'hema.


Pamenepo Mose anatenga mkazi wake ndi ana ake aamuna, nawakweza pabulu, nabwerera kunka ku dziko la Ejipito; ndipo Mose anagwira ndodo ya Mulungu m'dzanja lake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa