Eksodo 17:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo Mose anamanga guwa la nsembe, nalitcha dzina lake Yehova Nisi: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo Mose anamanga guwa la nsembe, nalitcha dzina lake Yehova Nisi: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ndipo Mose adamanga guwa nalitcha kuti, “Chauta ndiye mbendera yanga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Mose anamanga guwa lansembe ndipo analitcha Yehova Chipambano Changa (Yehova Nisi). Onani mutuwo |