Eksodo 17:16 - Buku Lopatulika16 nati, Yehova walumbira: padzakhala nkhondo ya Yehova pa Amaleke m'mibadwomibadwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 nati, Yehova walumbira: padzakhala nkhondo ya Yehova pa Amaleke m'mibadwomibadwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Adati, “Kwezetsani mbendera ya Chauta! Chauta adzapitirirabe kumenya nkhondo ndi Aamaleke mpaka muyaya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndipo anati, “Kwezani mbendera ya Yehova. Yehova adzachitabe nkhondo ndi mibado yonse ya Aamaleki.” Onani mutuwo |