Eksodo 17:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo Yoswa anathyola Amaleke ndi anthu ake ndi ukali wa lupanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo Yoswa anathyola Amaleke ndi anthu ake ndi ku ukali kwa lupanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ndipo Yoswa adagonjetseratu kwathunthu Aamalekewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Kotero Yoswa anagonjetsa asilikali ankhondo a Amaleki ndi lupanga. Onani mutuwo |