Eksodo 16:26 - Buku Lopatulika26 Muziola uwu masiku asanu ndi limodzi; koma tsiku lachisanu ndi chiwiri ndilo la Sabata, pamenepo padzakhala palibe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Muziola uwu masiku asanu ndi limodzi; koma tsiku lachisanu ndi chiwiri ndilo la Sabata, pamenepo padzakhala palibe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Mutole chakudya pa masiku asanu ndi limodzi. Koma pa tsiku lachisanu ndi chiŵiri, tsiku la Sabata, chakudyacho sichidzapezeka.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Muzitola chakudya masiku asanu ndi limodzi koma tsiku la chisanu ndi chiwiri ndi la Sabata, simukapeza chilichonse kunjaku.” Onani mutuwo |