Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 16:27 - Buku Lopatulika

27 Ndipo kunali tsiku la Sabata, kuti anthu ena anatuluka kukaola, koma sanaupeze.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Ndipo kunali tsiku la Sabata, kuti anthu ena anatuluka kukaola, koma sanaupeze.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Pa tsiku lachisanu ndi chiŵirilo anthu ena adaapita kuti akatole chakudya, koma sadachipeze.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Komabe anthu ena anapita kuti akatole chakudya tsiku lachisanu ndi chiwiri, koma sanapeze kanthu.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 16:27
3 Mawu Ofanana  

Muziola uwu masiku asanu ndi limodzi; koma tsiku lachisanu ndi chiwiri ndilo la Sabata, pamenepo padzakhala palibe.


Ndipo Yehova anati kwa Mose, Mukana kusunga zouza zanga ndi malamulo anga kufikira liti?


Waulesi salima chifukwa cha chisanu; adzapemphapempha m'masika osalandira kanthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa