Eksodo 16:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Mukana kusunga zouza zanga ndi malamulo anga kufikira liti? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Mukana kusunga zouza zanga ndi malamulo anga kufikira liti? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Pamenepo Chauta adafunsa Mose kuti, “Kodi mudzakhalabe osamvera mau anga ndi malamulo anga mpaka liti? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Ndipo Yehova anafunsa Mose nati, “Kodi inu muzipitirira kukana kusunga malamulo ndi malangizo anga mpaka liti? Onani mutuwo |