Eksodo 15:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo anthu anadandaulira Mose, ndi kuti, Tidzamwa chiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo anthu anadandaulira Mose, ndi kuti, Tidzamwa chiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Apo anthu aja adadandaulira Mose, namufunsa kuti, “Kodi ife timwa chiyani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Tsono anthu aja anadandaulira Mose ndi kumufunsa kuti, “Kodi tikumwa chiyani?” Onani mutuwo |