Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 15:23 - Buku Lopatulika

23 Pamene anafika ku Mara sanakhoze kumwa madzi a pa Mara, pakuti anali owawa; chifukwa chake anatcha dzina lake Mara.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Pamene anafika ku Mara sanakhoze kumwa madzi a Mara, pakuti anali owawa; chifukwa chake anatcha dzina lake Mara.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Ndipo adakafika ku Mara, koma kumeneko madzi ake anali oŵaŵa, kotero kuti sadathe kuŵamwa. Nchifukwa chake malowo adaŵatcha kuti Mara.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Ndipo anafika ku Mara. Koma sanathe kumwa madzi akumeneko chifukwa anali owawa. (Ndi chifukwa chake malowo amatchedwa Mara).

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 15:23
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anachokera ku Pihahiroti, naoloka pakati pa nyanja nalowa m'chipululu; nayenda ulendo wa masiku atatu m'chipululu cha Etamu, namanga mu Mara.


Koma ananena nao, Musanditcha Naomi, munditche Mara; pakuti Wamphamvuyonse anandichitira zowawa ndithu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa