Eksodo 15:14 - Buku Lopatulika14 Mitundu ya anthu idamva, inanthunthumira; kuda mtima kwagwira anthu okhala mu Filistiya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Mitundu ya anthu idamva, inanthunthumira; kuda mtima kwagwira anthu okhala m'Filistiya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Anthu a mitundu ina amva mbiriyi, ndipo anjenjemera ndi mantha. Mantha oopsa aŵagwira Afilisti. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Anthu amitundu ina anamva za mbiriyi ndipo ananjenjemera ndi mantha, mantha woopsa agwira anthu a dziko la Filisiti. Onani mutuwo |