Eksodo 15:13 - Buku Lopatulika13 Mwa chifundo chanu mwatsogolera anthu amene mudawaombola; mwamphamvu yanu mudawalondolera njira yakunka pokhala panu poyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Mwa chifundo chanu mwatsogolera anthu amene mudawaombola; mwamphamvu yanu mudawalondolera njira yakunka pokhala panu poyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 “Koma anthu amene mudaŵaombola, mudaŵatsogolera ndi chikondi chanu chosasinthika. Mudaŵatsogolera ku malo anu oyera ndi mphamvu zanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndi chikondi chanu chosasinthika mudzatsogolera anthu amene munawawombola. Ndi mphamvu zanu munawatsogolera ku malo anu woyera. Onani mutuwo |