Eksodo 14:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo kunali, ulonda wa mamawa, Yehova ali m'moto ndi m'mtambo njo anapenyera pa ulendo wa Aejipito, nauvuta ulendo wa Aejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo kunali, ulonda wa mamawa, Yehova ali m'moto ndi m'mtambo njo anapenyera pa ulendo wa Aejipito, nauvuta ulendo wa Aejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Tsono kusanache m'maŵa ndithu, Chauta, ali m'chipilala chamtambo ndi chamoto, adayang'ana ankhondo a Aejipito ndipo adaŵachititsa mantha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Kutatsala pangʼono kucha, Yehova ali mu chipilala chamoto ndi chamtambo, anayangʼana asilikali ankhondo a Igupto ndipo anabweretsa chisokonezo pakati pawo. Onani mutuwo |